Kusabereka mu Utumiki

Kusabereka ndi chifukwa chosowa zipatso zenizeni mu mpingo wachiKhristu wamakono. Pali ntchito zambiri komanso mapulogalamu ambiri koma pali zipatso zochepa kapena palibe. Pali zambiri ku utumiki kuposa kupeza ziphaso zambiri za chidziwitso cha Baibulo. Abusa ambiri amagwa mu ulendo wawo chifukwa chokhumudwa komanso kunyengedwa chifukwa chakuti ndi osabala mu utumiki. Mulungu amafuna kuti tizibala zipatso. Mulungu akufuna kuti tiwonjezekere mu utumiki. Kuti mubereke muyenera kumvetsetsa kuti kusabereka kumatanthauza chiyani. Kusabereka ndi vuto lomwe Mulungu akufuna kuthana nalo mu utumiki wanu. Bukhu lapanthawi yake limeneli, lolembedwa ndi Dag Heward-Mills lidzakuthandizani kuleka kusabereka mu utumiki wanu. Mzimu wosabereka ukachotsedwa mudzayamba kubala zipatso. Mukutuluka mu kusabereka lero!

Category:

Description

Kusabereka ndi chifukwa chosowa zipatso zenizeni mu mpingo wachiKhristu wamakono. Pali ntchito zambiri komanso mapulogalamu ambiri koma pali zipatso zochepa kapena palibe. Pali zambiri ku utumiki kuposa kupeza ziphaso zambiri za chidziwitso cha Baibulo. Abusa ambiri amagwa mu ulendo wawo chifukwa chokhumudwa komanso kunyengedwa chifukwa chakuti ndi osabala mu utumiki. Mulungu amafuna kuti tizibala zipatso. Mulungu akufuna kuti tiwonjezekere mu utumiki. Kuti mubereke muyenera kumvetsetsa kuti kusabereka kumatanthauza chiyani. Kusabereka ndi vuto lomwe Mulungu akufuna kuthana nalo mu utumiki wanu. Bukhu lapanthawi yake limeneli, lolembedwa ndi Dag Heward-Mills lidzakuthandizani kuleka kusabereka mu utumiki wanu. Mzimu wosabereka ukachotsedwa mudzayamba kubala zipatso. Mukutuluka mu kusabereka lero!

Reviews

There are no reviews yet.

Be the first to review “Kusabereka mu Utumiki”

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Title

Go to Top