…ndipo pomwepo chidzafika chimaliziro. Mateyu 24:14
Ndi chiyani chomwe chingathetse moyo monga mukudziwira? Kodi ndi mphamvu yanji yopangitsa kutha kwa zinthu zonse m’moyo wanu? Kodi chizindikiro cha kutha kwa utumiki wanu padziko lapansi chidzakhala chiyani? Kodi n’chiyani chidzathetse mpingo? Mapeto a chilichonse ndi imfa!
Anthu ambiri otchulidwa m’bukhuli anatha momvetsa chisoni. Ndikofunika kudziwa chifukwa chomwe moyo wawo unathera. Ndikofunika kudziwa chifukwa chomwe mautumiki a anthu amathera.
Kupyolera mu bukhu lounikirali, mudzaona kuti kudzikuza, kusamvera, chidani, kupotoza, kupanduka ndi kunyoza ndi zina mwa zinthu zosasangalatsa zimene zingawononge moyo wanu ndi utumiki wanu.
Utumiki wanu uwomboledwe mathero a m’njira yatsoka mofananamo pamene mulandira nzeru zazikulu kuchokera m’bukhu losonkhezera maganizo limeneli.

Reviews
There are no reviews yet.