Mfundo ndi chivumbulutso! Mfundo ndi chinachake chimene chimakulola kuti ukule! Mfundo ndi kumvetsa mozama mmene chinthu chimagwirira ntchito.
Bukuli lili ndi mfundo zosiyanasiyana, zonse zokhudzana ndi chipulumutso chachikulu chimene takumana nacho mwa Khristu!
Lolowerani mozama pa kumvetsa kwanu chipulumutso pamene mukuphunzira mfundo zazikulu zisanu ndi ziwiri izi. Pamene mukuchita zimenezi, Mulungu adzaika m’manja mwanu makiyi amene adzakutsimikizirani kukwera m’magulu apamwamba kwambiri mwa Iye.

Reviews
There are no reviews yet.