-
พระคัมภีร์ให้รายชื่อที่เหมาะสมของพวกศัตรูซึ่งมองไม่เห็นแก่เรา เป็นหน้าที่ของเราที่จะเชื่อพระวจนะของพระเจ้าและต่อสู้แต่ละตัวของพวกมันจนกระทั่งเราบดขยี้พวกมันภายในเท้าของเรา อย่าประเมินความเป็นจริงของโลกวิญญาณต่ำไป โลกวิญญาณเป็นโลกที่แท้จริง โลกนี้เป็นโลกที่ชั่วคราว (ไม่เป็นจริง) นี่คือรายชื่อของพวกศัตรูซึ่งมองไม่เห็นที่คุณต้องคาดหวังที่จะเผชิญหน้าในขณะที่คุณดำเนินชีวิตในโลกนี้ พระเยซูไม่ได้ไปไกลก่อนที่พระองค์ได้เผชิญหน้ากับพวกมาร พระองค์ได้เผชิญหน้ากับพวกมารตลอดชีวิตและพันธกิจในโลกนี้ของพระองค์
-
Perëndia ka thirrur shumë njerëz me të vërtetë. Jeta jonë në tokë është një mundësi për t’i shërbyer Atij dhe Perëndia vështron gjërat që po bëni për Mbretërinë e tij. Ky libër përbën një lexim stimulues. Nëse i përvetësoni të vërtetat e përçuara nga autori, do të merrni urtësi për të përdorur mundësitë e jetës suaj në mënyrën e duhur.
-
Mu bukhu lapamwambali, Dag Heward-Mills akupereka kuzindikira kwakukulu kwa zochitika m'banja. Bukhu lodabwitsali likagwira ntchito ngati chipangizo chokonzekera kwa phungu wa banja ndi anthu okwatira. Inu mukapeza mu bukhuli, mfundo zotsitsimutsa ndi zosangalatsa zopititsa patsogolo banja lanu. "Bukhu ili ndilodzadza ndi nkhani pa maziko ndi zochitika pa maubwenzi a umunthu mu nthawi imene musanakwatire, muli m'banja ndi ngakhale utatha ukwati. Ili ndi zipangizo zofufuzidwa bwino ndi zovomerezeka pa thunthu ndi kakhalidwe kazolengedwa pazogonana, kubereka kwa anthu, mimba ndi nthawi yobereka ikadutsa. Kuthekera kwa Dotolo Dag Heward-Mills kusintha nkhani zovuta kukhala zophweka ndiye chikhalidwe chosiyanitsa pa bukhuli. Zonse pamodzi, izi zimalipangitsa kukhala bukhu losindikizika lomveka kwambiri, logwiritsika ntchito bwino pa zabanja lero." David Asomani, katswiri wowona za chiberekero cha azimayi. "Bukhu la Bishopu Dag Heward-Mills pa uphungu wa m'banja ndilosowa chifanizo. Maziko ake ngati dotolo wa zachipatala zawonetsedwa momveka bwino mu tsatanetsatane, koma kudzifotokozera kwa zizindikiro zachipatala zomwe zikupangitsa bukhuli kukhala lapadera." Edwin Morgan Ogoe, Mphunzitsi, Sukulu Yaukachenjede ya Ghana, Sukulu Yazachipatala
-
Baibulo limatiuza kuti tonse timalakwitsa- Abusa nawo amalakwitsanso. Kulakwitsa kumabwezeretsa m’mbuyo. Kulakwitsa kumalepheretsa kupita chitsogolo. Kodi ndi zolakwitsa ziti zimene abusa anu apanga? Kodi ndi chiyani chingakhale zolakwitsa zazikulu khumi zimene abusa amachita? Muli omasuka kuwerenga Bukuli ndi kuzindikira zolakwika zimene mungazichite ndi m'mene mungazipewere. Buku lofunikali lidzakhala mdalitso kwa inu ndi utumiki wanu.