-
Bukhu limeneri ndi chotsatira chomwe chadikiridwa kwambiri cha “M’busa Wamba ndi Utumiki”. Kumaimira kusiyana kwa pakati pa utumiki wa munthu wamba ndi utumiki wa nthawi zonse. Mu bukhu lapaderali Dag Heward-Mills akukulimbikitsani kuti mukadzipereke nokha kwa thunthu kwa Mulungu ndi kukupangitsani kupeza zifukwa zoyenera zolowera mu utumiki wa nthawi zonse.
-
Tonse timalindirira moyo waulemerero komwe kuzakhala "KULIBENSO THEMBERERO!" Ichi ndi chifukwa choti mmoyo timakumana ndi matsoka, kuzunzika kopitirira, utsiru, kusasangalala ndi kukhumudwa. Themberero limafotokoza bwino matsoka okumana nawowa omwe tikuwoneka kuti timakumana nawo. Tingazipewe? Pali njira yosakumanirana nazo? Bukhuli likakuthandizani inu kumvetsetsa matemberero ndi momwe mungazikhadzikitsire nokha kuti mukalandire mdalitso.
-
Bukhu latsopanoli, "Malamulo a Ntchito ya Mpingo", ndi chida chofunikira kwambiri kwa amene ali ndi chikhumbokhumbo chogwilira ntchito mu tchalitchi. Dag Heward-Mills, mu kalembedwe kake ka nthawi zonse, akupeleka malamulo ogwilira mu utumiki wa nthawi zonse komanso kubweletsa bvumbulutso lofunikira kwambiri pa kuchita bwino mu utumiki.
-
A Keresztényekre számos veszély, kelepce és csapda leselkedik. Ez a könyv felnyitja szemeteket azon számos alattomos veszélyre, amelyek csak arra várnak, hogy bánthassanak, megsebesíthessenek és megsemmisíthessenek minket. Segíts magadon, mentsd meg magadat és szabadítsd fel magadat a szellemi veszélyekről szóló erőteljes könyv segítségével. -
Ngati Mkhristu, chikoka chachikulu komanso chokometsetsa mu moyo wanu chikuyenera kukhala Mzimu Woyera. Bukhuli likukulolani kumvetsetsa khalidwe lanu, kuzindikira kwanu, luso lanu ndinso kuthekera kwanu kokhala woyera kutha kukokedwa ndi Mzimu Woyera. Kudzera mu bukhu lapamwambali lolembedwa ndi Dag Heward-Mills, mukuyenera kulola Mzimu Woyera kukukokani, kukulimbikitsani, kukukhadzani komanso kusintha moyo wanu kwa muyaya.
-
Bukhu lija la abusa ndi akazi a abusa lafika! Bukhu ili silikhudza inu ngati sindinu mbusa kapena mkazi wa mbusa! Ngati inu muli oyenerezeka kuwerenga bukuli, muloleni Mulungu akutumikireni inu mu buku loshosha maganizoli. Mu masambawa, maudindo achinsinsi omwe akazi achita mu miyoyo ya azibusa awululika. Masambawa akulangizeni inu ndi kukudzetsani inu m'njira ya mdalisto!
-
Bukhuli lizachiza kusweka mitima kwa ana aakazi! Mubukhu loyembekezerekali, akazi akulimbikitsika kulola nzeru ya Mulungu kuwathandiza iwo kugonjetsa zinthu zosatheka zambiri zomwe amakumana nazo. Mulungu adzakhuza moyo wanu ndi kulimbikitsa inu pamene mukulimva bwino bukhu lamphamvu latsopanoli maka maka kwa ana aakazi.
-
Moyo ungakhale wovuta kwa aliyense. Nthawi zambiri chomwe mukufuna kuti mugonjetse chomwe inu mwagwamo ndi nzeru. Nzeru ndi chinsinsi cha Mulungu chomwe chikuthandizeni inu kuwuka kuchokera nkulimbana ndikukhala chozizwitsa chamoyo. Mulungu wakuikani inu ku ulemerero. Chinsinsi cha Mulungu ndi nzeru ya Mulungu mu chinsinsi chomwe chaikidwa pa ulemerero ndi kukongola kwanu. Zibvumbulutso za bukhuli zikubweretsereni chigonjetso tsiku lililonse! Bukhu ili likupatseni chidziwitso ndi kupambana!