Talán már hallottad, hogy nagyszerű dolog az Urat szolgálni; azonban, lehetséges, hogy nem gondoltad át alaposan, hogy milyen nagyszerű dolog az Urat, a mi Istenünket szolgálni. Dag Heward-Mills egyedi könyve bemutatja ki az Isten szolgálója és hogyan szolgálhatod az Urat.Megértheted a gyakorlati különbséget az Urat szolgálók és az Urat elutasítók között! Csatlakozz az Urat szolgálók közé! Megértheted a gyakorlati különbséget az Urat szolgálók és az Urat elutasítók között! Csatlakozz az Urat szolgálók közé! |
-
-
Dag Heward-Mills ni mwandishi wa vitabu vingi, ikiwemo kitabu kinachouzwa sana "Uaminifu na Ukosefu wa Uaminifu". Yeye ni mwanzilishi wa dhehebu lenye makanisa zaidi ya elfu moja linaloitwa "The Lighthouse Chapel International". (Kanisa la Kimataifa la Lighthouse). Dag Heward-Mills, mwinjilisti wa kimataifa huhudumu katika Mkutano wa Injili wa Kimataifa na Yesu Mponyaji na mikutano duniani kote. kwa taarifa zaidi, tembelea www.daghewardmills.org.
-
Bukhuli lizachiza kusweka mitima kwa ana aakazi! Mubukhu loyembekezerekali, akazi akulimbikitsika kulola nzeru ya Mulungu kuwathandiza iwo kugonjetsa zinthu zosatheka zambiri zomwe amakumana nazo. Mulungu adzakhuza moyo wanu ndi kulimbikitsa inu pamene mukulimva bwino bukhu lamphamvu latsopanoli maka maka kwa ana aakazi.
-
Mu buku lopambanali, Dag Heward-Mills akusanthula zinthu zochitikadi mu utumiki masiku ano. Akukamba za zinthu zochitika zokhudza zachuma, ndale, kucheza ndi amuna kapena akazi komanso maubale mu utumiki. Bukuli ndi muuni wa makhalidwe otsatira mwambo pa mayitanidwe anu ndipo ndi buku lomwe mtsogoleri wachikhristu aliyense akuyenera kukhala nalo. Ndi lovomerezeka ku sukulu za Baibulo ndi kwa atumiki onse.
-
Mau opatsa chidwi amenewa mwa inu mmodzi ndi mdierekezi" analankhulidwa ndi Yesu Khristu pa gulu lake lalingono la ophunzira khumi ndi awiri. Ambiri a ife timachitiridwa zowawa ndi mdierekezi chifukwa sitimadziwa momwe tingamuonetsera poyera kapenanso kukazindikira zintchito zake. Mu bukhu lodalitsika limeneli, mudzatulukira uchimo wa mdierekezi ndi kupanga chisankho cha kusayenda mmenemo. Zikhale kuti mau awa mwa inu mmodzi ndi mdierekezi asakhale akunenera pa inu!
-
Adesea suntem bucuroşi când ne gândim la faptul că "mulți sunt chemați". Apoi, prea devreme, devenim entuziasmați atunci când medităm asupra faptului că "... puțini sunt aleși". Puteți fi printre cei mulți care sunt chemați și puținii care sunt aleși dacă faceți această carte o parte a vieții voastre. În această carte uimitoare scrisă de Dag Heward-Mills, veți afla din Biblie de ce puteți spune cu încredere că sunteți chemați. Veți cunoaște caracteristicile oamenilor chemați și veți fi încurajați să fiți statornici până la sfârșitul cursei creștine.
-
Iki gitabo kirakiza ibikomere abakobwa! Muri iki gitabo cyari gitegerejwe na benshi, Abagore barasabwa kwemera kuyoborwa nubwenge bw'Imana kugirango bibafashe gutsinda ibibazo bitoroshye bahura nabyo. Imana izakora kubuzima bwawe uko ujyenda unezezwa na kino gitabo cyuzuye imbaraga cyagenewe byumwihariko abakobwa.
-
Deus tem chamado muitas pessoas de fato. A nossa vida na Terra é uma oportunidade de servi-Lo , e Deus está de olho nas coisas que você está fazendo para o seu Reino. Este livro faz uma leitura estimulante. Se você absorver as verdades transmitidas pelo autor, você receberá sabedoria para aproveitar as oportunidades de sua vida no caminho certo . Possuir sua cópia por encomenda online agora.
-
Dios ha llamado a mucha gente. Nuestra vida en la tierra es una oportunidad para servirle a Él, y Dios tiene puesto Su ojo en las cosas que estás haciendo para Su reino. Este libro es una lectura estimulante. Si absorbes las verdades expresadas por el autor, recibirás la sabiduría para utilizar las oportunidades de tu vida en la forma correcta.
-
Dag Heward-Mills ni mwandishi wa vitabu vingi, ikiwemo kitabu kinachouzwa sana "Uaminifu na Ukosefu wa Uaminifu". Yeye ni mwanzilishi wa dhehebu lenye makanisa zaidi ya elfu moja linaloitwa "The Lighthouse Chapel International". (Kanisa la Kimataifa la Lighthouse). Dag Heward-Mills, mwinjilisti wa kimataifa huhudumu katika Mkutano wa Injili wa Kimataifa na Yesu Mponyaji na mikutano duniani kote. kwa taarifa zaidi, tembelea www.daghewardmills.org.
-
Anthu ambiri samamvetsetsa za malo a mtengo wa dzindikila chabwino ndi choipa m`moyo mwathu. Nthawi zambiri timaganiza kuti unali mtengo qmwe unalipo kalekale munthawi ya Adamu ndi Eva. Timakhulupirira kuti mtengo umeneyo unali ndi zipatso za poizoni zoti ukangodya yemwe wadyayo amafa. Mwa tsoka, Adamu ndi Eva anadya za mtengowu ndipo anafa. Tikawerenga za nkhaniyi, timaganiza kwa ife, “zinali zomvetsa chisoni Adam ndi Eva kudya chipatso chakuphachi koma tithokoze sitidzaikidwa m`mayeselo ndi mtengo ngati umenewo”. Zachisoni, tikhala tikulimbana ndi mtengo umenewu ndi zipatso zake. Chomwe tiyenera kudziwa ndi chakuti za mtengo wa kudzindikira chabwino ndi choipa udakalipobe mpaka lero. Umagwira ntchito m`mayesero kwa ife chimodzimodzi m`mene unapangira nthawi ya Adamu ndi Eva. Umayimilira ngati njira ina ya kwa Mulungu.