-
Azibusa ali pa mpani pani wokondweretsa ndi kusangalatsa anthu awo ndi uthenga wabwino. Mpani pani wa anthu umenewu wapangitsa kusintha kwa mawu a Khristu kufikira mawu a mtanda akhalira kovuta kuzindikirika. Lero, tikubwerera ku maziko a chilungamo cha Chikhristu choti tikuyenera “kutaya” kuti “tipeze” Khristu. Mphamvu izabwerera ku mpingo pamene tikulalikira kuti tipereke nsembe, kusautsidwa ndi kufa chifukwa cha Khristu. Mphamvu ya mawu a Khristu siingafufutidwe ndi wina aliyense posatengera kuchita bwino kapena kukhala wa mphamvu.
-
Dag Heward-Mills ni mwandishi wa vitabu vingi, ikiwemo kitabu kinachouzwa sana "Uaminifu na Ukosefu wa Uaminifu". Yeye ni mwanzilishi wa dhehebu lenye makanisa zaidi ya elfu moja linaloitwa "The Lighthouse Chapel International". (Kanisa la Kimataifa la Lighthouse). Dag Heward-Mills, mwinjilisti wa kimataifa huhudumu katika Mkutano wa Injili wa Kimataifa na Yesu Mponyaji na mikutano duniani kote. kwa taarifa zaidi, tembelea www.daghewardmills.org.
-
Embora o diabo é comumente conhecido como o acusador dos irmãos, ele é realmente o acusador no meio dos irmãos. Em sua experiência de liderança, você vai conhecer diferentes tipos de pessoas. Talvez um dos inimigos mais assustadores que você nunca vai encontrar é "o acusador no meio dos irmãos". Saiba mais nesta nova versão por Dag Heward-Mills
-
Wachungaji wanashinikizwa kuwafurahisha na kuwapendeza washirika wao kwa habari njema. Shinikizo hii ya watu imesababisha kubadilisha kwa maneno ya Kristo mpaka imekuwa vigumu kutambua ujumbe wa msalaba. Leo, tunarudi kwa ukweli wa msingi wa Ukristo kwamba tunapaswa "kupoteza" ili "kumpata" Kristo. Nguvu itarudi katika kanisa kadiri tunavyohubiri kwamba tunapaswa kujitoa dhabihu, kuteseka na kufa kwa ajili ya Kristo. Nguvu ya maneno ya Kristo haiwezi kuondolewa na mtu yeyote hata kama amefanikiwa au ni mtu wa nguvu namna gani.
-
Kudzoza ndi chifungulo chachichikulu chofunikira kutsegula khomo la kuchita bwino ndo kukwaniritsa utumiki. Anthu ambiri ayesera kuchita ntchito ya Mulungu chifukwa cha mafuno abwino, popanda kufika kutali analephera kuzindikira kuti “Ndi khamu la nkhondo ai, ndi mphamvu ai, koma ndi Mzimu Wanga (Kudzoza)” [Zekariya 4:4]. Bukhu lapderali “Kupeza Kudzoza” lolembedwa ndi Bishopu Dag Heward-mills lizakuphunzitsani inu zomwe zimatanthauza kupeza kudzoza ndi momwe mungapangire! Lolani chikhumbo khumbo cha Kudzoza kwa Mulungu kutakasike mkati mwanu kudzera mu masamba a m’bukhuli!
-
Tegenwoordig zijn er veel kleine dingen die we kunnen doen die een enorm verschil zullen maken in de algehele inspanning om het koninkrijk van God op te bouwen. Gewoon een beetje meer moeite, een beetje meer tijd, een beetje meer geld om de zaak van Christus te bevorderen, een beetje meer interesse in de ongeremde ziel, een beetje meer zorg voor uw naaste zal een enorm verschil maken. Kunt u niet een beetje meer doen? Dit is een klaroengeschal die we niet kunnen negeren! Kunt u niet nog een beetje meer doen?
-
Kāpēc Visvarenajam Dievam kāds būtu vajadzīgs? Ko Tas Kungs no tevis vēlētos? Kas ir tas, ko Dievs nevar izdarīt pats? Ko Dievs nevar panākt pats? Dievs meklē kādu, kas nostātos starp Viņu un cilvēku. Dievs meklē kādu, kas atbildētu uz mazo cilvēku jautājumiem! Dievs meklē kādu, kas atbrīvotu bērnus, kuri ir tālu no drošības! Bībele saka, ka Dievs meklēja cilvēku…! Izmantojot šo sirdi sildošo grāmatu, jūsu vēlme būt labprātīgam traukam Dieva rokās palīdzēs jums to veicināt! Jūs vairs neapmierināsieties ar to, ka esat vienkāršs draudzes loceklis. Jūs kļūsiet par palīgu!
-
Tikudziwa kui kukula kwa mpingo ndi chinthu chovuta kukwaniritsa. azibusa onse amafuna mpingo wawo ukule. bukhuli ndi yankho la kufuna kwanu kwa kukula kwa mpingo. mukamvetsetsa momwe "zinthu zosiyanasiyana zimawirira pamodzi" kukwaniritsa kukula kwa mpingo. wokondedwa m'busa, pomwe mawu ndi kudzoza kuli m'bukhuli kukubwera mu mtima mwanu, muzakhala ndi kukula kwa mpingo komwe mwakhala mukupempherera.
-
Bukhu lija la abusa ndi akazi a abusa lafika! Bukhu ili silikhudza inu ngati sindinu mbusa kapena mkazi wa mbusa! Ngati inu muli oyenerezeka kuwerenga bukuli, muloleni Mulungu akutumikireni inu mu buku loshosha maganizoli. Mu masambawa, maudindo achinsinsi omwe akazi achita mu miyoyo ya azibusa awululika. Masambawa akulangizeni inu ndi kukudzetsani inu m'njira ya mdalisto!
-
Ingakhale ndi chofunikira choyamba cha Mulungu kwa atsogoleri, zochepa kwambiri zalembedwa pa mutu uwu. Mu bukhuli, Dag Heward-Mills akutchula mfundo zikulu zikulu ndi cholinga chokulitsira kukhadzikika kwa matchalitchi. Zamkati mwa bukhuli zili zoyenerera komanso zochitika mpaka ndi kukhala chida chosasiidwa kwa atsogoleri ambiri.