-
Те, що «багато покликаних», надихає, а те, що «вибраних мало», розчаровує. Дізнайтесь із цієї книги, як стати одним із покликаних і вибраних. Автор показує, як, спираючись на Біблію, можна набути впевненість у своєму покликанні. Ви дізнаєтесь характеристики «покликаних» і будете заохочені непохитно прямувати у своєму християнському поприщі.
-
Pastoři jsou pod neustálým tlakem, aby na svou kongregaci udělali dojem a přinesli jí dobré zprávy. Kvůli tomuto tlaku lidé často Kristova slova překrucují, až poselství kříže téměř vymizí. Dnes se navracíme k základům křesťanství, které tvrdí, že pokud chceme něco „získat“, musíme nejprve něco „ztratit.“ Když budeme kázat, že se musíme obětovat, trpět a zemřít pro Krista, církvi se navrátí síla. Síla Kristových slov nemůže být nikým vymazána, nehledě na to, jak úspěšný či mocný ten člověk je.
-
Chinthu chimodzi chokha chimadza kwa inu mukamva mawu akuti "M’busa" - nkhosa! Nkhosa ndi nyama zodalira zome zimafunikira abusa. M’busa ndi wotsogolera wosamalira komanso wachikondi kwa nkhosa. M'Baibulo, Mulungu amatitchula ife ngati gulu la nkhosa za Mulungu. Yesu adamuuza wophunzira Petro kuti adyetse nkhosa zake kuti atsimikizire za chikondi chake cha Mpulumutsi. Kukhala m'busa ndi ntchito yabwino kwambiri. Ndi chinthu chapamwamba kuitanidwa ndi Mulungu ndi kulembetsedwa mwa antchito Ake ndi kusamalira nkhosa. Mu bukhuli, Dag Heward-Mills akutiitanira ife, akutilimbikitsa ndi kutiwonetsa ife momwe tingatengerepo nawo mbali pa ntchito yayikulu yosamalira anthu a Mulungu. Musati muzisiyidwe kunja kwa ntchito yabwino iyi yokhala m’busa!
-
Baibulo limatiuza kuti tonse timalakwitsa- Abusa nawo amalakwitsanso. Kulakwitsa kumabwezeretsa m’mbuyo. Kulakwitsa kumalepheretsa kupita chitsogolo. Kodi ndi zolakwitsa ziti zimene abusa anu apanga? Kodi ndi chiyani chingakhale zolakwitsa zazikulu khumi zimene abusa amachita? Muli omasuka kuwerenga Bukuli ndi kuzindikira zolakwika zimene mungazichite ndi m'mene mungazipewere. Buku lofunikali lidzakhala mdalitso kwa inu ndi utumiki wanu.
-
Kodi Chimachitika Ndi Chiyani Mukabadwa Mwatsopano? Mzimu wa Mulungu azabwera pa inu, komanso mumtima mwanu. Kenako mkati mwanu mudzabadwa kapena kupangidwanso. Mulungu amakupatsani mtima watsopano ndi mzimu zonse! Ndi mzimu wanu watsopano, mumakhala munthu watsopano kapena cholengedwa chatsopano. Mwakonzeka kukhala moyo watsopano. Moyo watsopanowu ndiwotheka chifukwa ndiwe munthu watsopano wamtima watsopano. Kubadwa mwatsopano ndikosavuta monga choncho. Anthu amafuna kuchita zinthu zovuta. Koma kubadwanso mwatsopano ndikosavuta!
-
Gdy słyszysz słowo „pasterz”, tylko jedno przychodzi ci do głowy – owce! Owce są niesamodzielnymi stworzeniami, które potrzebują pasterzy. Pasterz jest troskliwym, kochającym przewodnikiem dla owiec. W Biblii Bóg mówi o nas jako owcach ze swego pastwiska. Jezus polecił również swojemu uczniowi Piotrowi paść Jego owce, aby okazał w ten sposób miłość Zbawicielowi. Bycie pasterzem jest bardzo ważną pracą. Zaszczytem jest być powołanym przez Boga do zasilenia szeregów Jego pracowników i troszczyć się o owce.
-
Moyo ungakhale wovuta kwa aliyense. Nthawi zambiri chomwe mukufuna kuti mugonjetse chomwe inu mwagwamo ndi nzeru. Nzeru ndi chinsinsi cha Mulungu chomwe chikuthandizeni inu kuwuka kuchokera nkulimbana ndikukhala chozizwitsa chamoyo. Mulungu wakuikani inu ku ulemerero. Chinsinsi cha Mulungu ndi nzeru ya Mulungu mu chinsinsi chomwe chaikidwa pa ulemerero ndi kukongola kwanu. Zibvumbulutso za bukhuli zikubweretsereni chigonjetso tsiku lililonse! Bukhu ili likupatseni chidziwitso ndi kupambana!