Mkhristu amayenda mkati kati mwa zoopsa zambiri ndi misampha. Bukhuli likatsekula maso anu ku zoopsa zambiri zobisika zomwe zikudikira kukupwetekani, kuvulaza komanso kuononga. Dzithandizeni nokha, dzipulumutseni nokha kudzera mu bukhu lamphamvu ili la zoopsa zauzimu!