-
"Katika kazi hii maalum, Dag Heward- Mills anatathmini hali halisi za maisha katika huduma leo. Anagusia mambo halisi kama fedha, siasa, kuhusiana na jinsi tofauti na mahusiano ya kihuduma. Mwongozo wa akili za kawaida kwa msingi halisi kwa wito wako, kitabu hiki ni cha lazima kwa kila kiongozi mkristo. Kinapendekezwa kwa hali ya juu kwa shule za Bibilia na makasisi kwa jumla."
-
Ce livre va guérir les blessures des filles ! Dans cet ouvrage longuement attendu, les femmes sont appelées à permettre à la sagesse de Dieu de les aider à surmonter de nombreuses situations difficiles auxquelles elles doivent faire face. Dieu vous touchera et vous fortifiera alors que vous lisez ce livre magnifique écrit spécialement pour les ‘filles’…
-
Kodi mukudziwa kuti aneneri akale, anafunsa ndi kufufuza zachipulumutso chachikuluchi chomwe chawonetseredwa kwa ife? Iwo sakanaganiza za momwe chipulumutsochi chingabwerere kwa anthu…koma ndife odalitsika kulandira chipulumutsochi! Ife talandira chipulumutso chifukwa winawake adatiuza za ichi. M'bukhu lopatsa chidwili, Mlaliki Dag Heward-Mills akutitsogolera ife kuti tisangomvetsetsa chipulumutso chathu chachikulu komanso mmene tingagawire ena uthenga wabwino wa chipulumutso chachikuluchi. Aliyense mwaife akachite ntchito ya mlaliki!
-
Palibe mwaife amene wayika dongosolo lokafika kumwamba opanda kuchita chomwe Mulungu amafuna kuti ife tikachite padziko lapansi. Ayi, olo ndi mmodzi! Ife tikufuna timalize ntchito Mulungu watipatsa ife. Bukhu ili ndilokhudza mmene mungakwanitsire utumiki wanu. Bukhu ili ndi kalondolondo ka momwe ife tingayankhire zochitika zaumulungu mmoyo mwathu - ndicholinga chosafuna kupezeka operewera patsikulo. Mukakwaniritse utumiki wanu ndipo Mulungu akanene kwa inu, "Wachita bwino, kapolo wabwino ndi okhulupirika!"
-
Ngati ndinu m’busa wa nkhosa za Mulungu, muzathandizika kwambiri ndi ntchito yabwinoyi. Masamba amenewa ali ndi malangizo ofotokozedwa bwino, ofunikira pa kuchita bwino kwanu. Bishop Dag Heward-Mills akutenga kuchokera mukukhala kwake kwa zaka zoposera makumi atatu ngati m’busa, kugawana nafe zinthu zochita mu ntchio ya utumiki. Ngati mwasirira kukhala m’busa wa anthu a Mulungu, iri ndi bukhu lokutsogolerani lomwe mwakhala mukulifuna.
-
Kutsatira Mulungu ndi ulendo wosangalatsa wopeza zinthu. Kutsatira ndi kutengera anthu ena ndi luso lachikale lophunzirira lomwe Yesu Khristu anasankha ngati njira yaikulu yophunzitsira. M’malo mochita manyazi ndi njira yoyesedwa ndi nthawiyi, ndi nthawi yomvetsetsa kukongola ndi kudzichepetsa kwa luso la kutsatira. Mu bukhuli, muzapeza yemwe, chomwe ndi momwe mungatsatire moyenerera. Bukhu lopambana latsopanoli lolembedwa ndi Dag Heward-Mills lipereka luso la kutsatira malo ake oyenerera mu zokumana zathu za Chikhristu.
-
Palibe mutu wofunikira kwambiri kuposa kukhala mu chifuniro cha Mulungu. Chokhacho chomwe chikasiyanitse azitumiki a uthenga ndi kuthekera kwawo kwa kumva mawu a Mulungu molondola. Momwe kulili kwabwino kutsatira Mzimu Woyera ku chifuniro cha Mulungu. Mukakhala mu chifuniro cha Mulungu, muzachita bwino ndipo muzakwaniritsa zokhumba zonse kwa Mulungu. Ntchito yapamwambayi yolembedwa ndi Dag Heward-Mills izakhala ndi kukhudza kwakukulu pa moyo wanu ndi utumiki.
-
“Taim yupela i sanap na mekim prea, na yupela i tingim wanpela rong wanpela man i bin mekim long yupela, orait YUPELA I MAS LUSIM RONG BILONG DISPELA MAN. OLSEM NA PAPA BILONG YUPELA I STAP LONG HEVEN EM BAI I LUSIM RONG BILONG YUPELA.” (Mak 11:25-26). Dispela 2pela ves mekim yup ret? Sapos em mekim yup ret, painim aut bilong yu stap long hia. Long dispela buk we nidim stret long en, yu bai lainim long lusim rong isi tasol – olsem na yu tu, Papa long heven bai lusim rong bilong yu. Mekim dispela buk kamap poro bilong yu i go inap yu ken lusim rong bilong ol lain isi tru na i no giman.
-
“Ol pasta save stap long bikpela wari long hamamas na hamamasim ol sios lain bilong ol wantaim gutnius. Na dispela wari bilong ol lain mekim ol kamap ting lus long toktok bilong Krais inap tok bilong diwai kros em go lus long ol Tude, yumi go bek long ol liklik tok tru bilong Kristen we yumi mas “lusim” long “kisim” Krais. Pawa bai kam bek gen long Sios taim yumi autim tok long yumi mas sekrifais, kisim hevi na dai long Krais. Nogat man inap long rausim pawa bilong tok bilong Krais, maski em wanem wanem kain man, em bai hat stret na bai i no inap.”
-
Kościoły pełne są idealnych zwodzicieli, którzy stają się idealnie nielojalni. Od zawsze główną sztuczką Szatana jest zwodzenie i pozory. Przywódca, który nie jest w stanie przejrzeć zwodziciela, będzie cierpiał z powodu swej ślepoty. Zastraszanie, poufałość i wprowadzanie w błąd to złe duchy, które atakują kapłanów. Przez większość czasu ludzie nawet nie są świadomi, że muszą z nimi walczyć. Ta książka pomoże ci rozpoznać i zwalczyć wroga, który przychodzi z wewnątrz.
-
"Ci, którzy cię opuszczają, mogą cię zniszczyć. Nic nie jest w stanie opisać smutku, zagubienia i niepokoju, które pojawia się, gdy ludzie od ciebie odchodzą. Ta książka została napisana, by pomóc ci pokonać tę destrukcję, związaną z byciem opuszczonym. Nie daj się zwieść. Nie przydarza się to tylko tobie. Wielu cierpiało z tego powodu. Szatan zbuntował się jako pierwszy i od tamtej pory inspiruje kolejne bunty. Dzięki tej książce podniesiesz się i zwalczysz ducha nielojalności, którego uwolnili „ci, którzy cię opuścili”.